Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 13:16 - Buku Lopatulika

Koma maso anu ali odala, chifukwa apenya; ndi makutu anu chifukwa amva.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma maso anu ali odala, chifukwa apenya; ndi makutu anu chifukwa amva.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Koma inu ndinu odala, popeza kuti maso anu akupenya, ndipo makutu anu akumva.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma maso anu ndi odala chifukwa amapenya ndi makutu anu chifukwa amamva.

Onani mutuwo



Mateyu 13:16
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anayankha iye, nati, Ndiwe wodala, Simoni Bara-Yona: pakuti thupi ndi mwazi sizinakuululire ichi, koma Atate wanga wa Kumwamba.


Yesu ananena kwa iye, Chifukwa wandiona Ine, wakhulupirira; odala iwo akukhulupirira, angakhale sanaone.


kukawatsegulira maso ao, kuti atembenuke kuchokera kumdima, kulinga kukuunika, ndi kuchokera ulamuliro wa Satana kulinga kwa Mulungu, kuti alandire iwo chikhululukiro cha machimo, ndi cholowa mwa iwo akuyeretsedwa ndi chikhulupiriro cha mwa Ine.


Pakuti Mulungu amene anati, Kuunika kudzawala kutuluka mumdima, ndiye amene anawala m'mitima yathu kutipatsa chiwalitsiro cha chidziwitso cha ulemerero wa Mulungu pankhope pa Yesu Khristu.