Yohane 20:29 - Buku Lopatulika29 Yesu ananena kwa iye, Chifukwa wandiona Ine, wakhulupirira; odala iwo akukhulupirira, angakhale sanaone. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Yesu ananena kwa iye, Chifukwa wandiona Ine, wakhulupirira; odala iwo akukhulupirira, angakhale sanaona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Yesu adati, “Kodi wakhulupirira chifukwa wandiwona? Ngwodala amene amakhulupirira ngakhale sadaone.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Kenaka Yesu anamuwuza kuti, “Kodi wakhulupirira chifukwa wandiona Ine? Ndi odala amene amakhulupirira ngakhale asanaone.” Onani mutuwo |