Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 1:10 - Buku Lopatulika

ndi Hezekiya anabala Manase; ndi Manase anabala Amoni; ndi Amoni anabala Yosiya;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Hezekiya anabala Manase; ndi Manase anabala Amoni; ndi Amoni anabala Yosiya;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Hezekiya adabereka Manase, Manase adabereka Amoni, Amoni adabereka Yosiya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Hezekiya anabereka Manase, Manase anabereka Amoni, Amoni anabereka Yosiya.

Onani mutuwo



Mateyu 1:10
8 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anafuula mwa mau a Yehova kutemberera guwa la nsembe, nati, Guwa la nsembe, guwa la nsembe, atero Yehova, Taona mwana adzabadwa m'nyumba ya Davide, dzina lake ndi Yosiya, adzaphera pa iwe ngati nsembe anthu ansembe a misanje, amene alikufukiza zonunkhira pa iwe, nadzatentha pa iwe mafupa a anthu.


Nagona Hezekiya ndi makolo ake; nakhala mfumu m'malo mwake Manase mwana wake.


Ndipo Hezekiya anagona ndi makolo ake, namuika polowerera kumanda a ana a Davide; ndi Ayuda onse ndi okhala mu Yerusalemu anamchitira ulemu pa imfa yake. Ndipo Manase mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


ndi Yosiya anabala Yekoniya ndi abale ake pa nthawi yakutengedwa kunka ku Babiloni.


ndi Uziya anabala Yotamu; ndi Yotamu anabala Ahazi; ndi Ahazi anabala Hezekiya;