Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 69:10 - Buku Lopatulika

Ndipo ndinalira pa kusala kwa moyo wanga, koma uku kunandikhalira chotonza.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ndinalira pa kusala kwa moyo wanga, koma uku kunandikhalira chotonza.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene ndidadzilanga posala zakudya, anthu adandinyoza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene ndikulira ndi kusala kudya, ndiyenera kupirira kunyozedwa;

Onani mutuwo



Masalimo 69:10
5 Mawu Ofanana  

Changu changa chinandithera, popeza akundisautsa anaiwala mau anu.


Koma ine, pakudwala iwowa, chovala changa ndi chiguduli. Ndinazunza moyo wanga ndi kusala; ndipo pemphero langa linabwera kuchifuwa changa.