Ndipo ndinalira pa kusala kwa moyo wanga, koma uku kunandikhalira chotonza.
Pamene ndidadzilanga posala zakudya, anthu adandinyoza.
Pamene ndikulira ndi kusala kudya, ndiyenera kupirira kunyozedwa;
Changu changa chinandithera, popeza akundisautsa anaiwala mau anu.
Koma ine, pakudwala iwowa, chovala changa ndi chiguduli. Ndinazunza moyo wanga ndi kusala; ndipo pemphero langa linabwera kuchifuwa changa.