Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 19:3 - Buku Lopatulika

Palibe chilankhulidwe, palibe mau; liu lao silimveka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Palibe chilankhulidwe, palibe mau; liu lao silimveka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Palibe kulankhula, palibe kunena mau aliwonse. Liwu lao silimveka konse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Palibe kuyankhula, palibe mawu aliwonse; liwu lawo silimveka.

Onani mutuwo



Masalimo 19:3
1 Mawu Ofanana  

ndi kuti mungakweze maso anu kupenya kumwamba, ndipo poona dzuwa ndi mwezi ndi nyenyezi, khamu lonse la kumwamba, munganyengedwe ndi kuzigwadira, ndi kuzitumikira, zimene Yehova Mulungu wanu anagawira mitundu yonse ya anthu pansi pa thambo lonse.