Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 2:3 - Buku Lopatulika

Ndipo anadza kwa Iye otenga munthu wodwala manjenje, wonyamulidwa ndi anthu anai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anadza kwa Iye otenga munthu wodwala manjenje, wonyamulidwa ndi anthu anai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu ena anai adaanyamula munthu wa ziwalo zakufa, kubwera naye kwa Yesu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amuna anayi anabwera, atanyamula munthu wofa ziwalo.

Onani mutuwo



Marko 2:3
3 Mawu Ofanana  

Ndipo mbiri yake inabuka ku Siriya konse: ndipo anatengera kwa Iye onse akudwala, ogwidwa ndi nthenda ndi mazunzo a mitundumitundu, ndi ogwidwa ndi ziwanda, ndi akhunyu, ndi amanjenje; ndipo Iye anawachiritsa.