Ndipo Hiramu mfumu ya ku Tiro anatuma anyamata ake kwa Solomoni, popeza anamva kuti adamdzoza mfumu m'malo mwa atate wake; pakuti Hiramu adakondana ndi Davide masiku onse.
Luka 7:5 - Buku Lopatulika pakuti akonda mtundu wathu, ndipo anatimangira ife sunagoge. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 pakuti akonda mtundu wathu, ndipo anatimangira ife sunagoge. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa chifukwa amaukonda mtundu wathu, mwakuti adatimangira nyumba yamapemphero.” Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero chifukwa amakonda mtundu wathu ndipo anatimangira sunagoge wathu.” |
Ndipo Hiramu mfumu ya ku Tiro anatuma anyamata ake kwa Solomoni, popeza anamva kuti adamdzoza mfumu m'malo mwa atate wake; pakuti Hiramu adakondana ndi Davide masiku onse.
Ndipo iwo, pakufika kwa Yesu, anampempha Iye koumirira, nati, Ayenera iye kuti mumchitire ichi;
Ndipo Yesu anapita nao. Ndipo pakufika Iye tsono pafupi pa nyumba yake, kenturiyo anatuma kwa Iye abwenzi ake, kunena naye, Ambuye, musadzivute; pakuti sindiyenera ine kuti mudzalowe pansi pa tsindwi langa;
Pakuti mwa Khristu Yesu kapena mdulidwe kapena kusadulidwa kulibe mphamvu; komatu chikhulupiriro, chakuchititsa mwa chikondi.
Ife tidziwa kuti tachokera kutuluka muimfa kulowa m'moyo, chifukwa tikondana ndi abale. Iye amene sakonda akhala muimfa.