Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 7:1 - Buku Lopatulika

Pamene Yesu adamaliza mau ake onse m'makutu a anthu, analowa mu Kapernao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamene Yesu adamaliza mau ake onse m'makutu a anthu, analowa m'Kapernao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu atatsiriza kulankhula zonsezi ndi anthu aja, adapita ku Kapernao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu atamaliza kunena zonsezi pamaso pa anthu amene ankamvetsera, analowa mu Kaperenawo.

Onani mutuwo



Luka 7:1
4 Mawu Ofanana  

Koma iye amene akumva, ndi kusachita, afanafana ndi munthu wakumanga nyumba pa nthaka yopanda maziko; pa imeneyo unagunda mtsinje, ndipo inagwa pomwepo; ndipo kugumuka kwake kwa nyumbayo kunali kwakukulu.