Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 3:6 - Buku Lopatulika

ndipo anthu onse adzaona chipulumutso cha Mulungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo anthu onse adzaona chipulumutso cha Mulungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero anthu onse adzaona chipulumutso chochokera kwa Mulungu.’ ”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anthu onse adzaona chipulumutso cha Mulungu.”

Onani mutuwo



Luka 3:6
9 Mawu Ofanana  

ndipo ulemerero wa Yehova udzavumbulutsidwa, ndipo anthu onse adzauona pamodzi, pakuti pakamwa pa Yehova panena chomwecho.


inde, ati, Chili chinthu chopepuka ndithu kuti Iwe ukhale mtumiki wanga wakuutsa mafuko a Yakobo, ndi kubwezera osungika a Israele; ndidzakupatsanso ukhale kuunika kwa amitundu, kuti ukhale chipulumutso changa mpaka ku malekezero a dziko lapansi.


Yehova wavula mkono wake woyera pamaso pa amitundu onse; ndi malekezero onse a dziko lapansi adzaona chipulumutso cha Mulungu wathu.


Ndipo ananena nao, Mukani kudziko lonse lapansi, lalikirani Uthenga Wabwino kwa olengedwa onse.


Pakuti kulibe kusiyana Myuda ndi Mgriki; pakuti Yemweyo ali Ambuye wa onse, nawachitira zolemera onse amene aitana pa Iye;


Koma ine nditi, Sanamva iwo kodi! Indetu, Liu lao linatulukira kudziko lonse lapansi, ndi maneno ao ku malekezero a dziko lokhalamo anthu.