Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 20:3 - Buku Lopatulika

Ndipo anayankha, nati kwa iwo, Ndidzakufunsani mau Inenso; mundiuze:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anayankha, nati kwa iwo, Ndidzakufunsani mau Inenso; mundiuze:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adati, “Nanenso ntakufunsani funso limodzi. Tandiwuzani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anayankha kuti, “Inenso ndikufunsani, mundiyankhe,

Onani mutuwo



Luka 20:3
5 Mawu Ofanana  

ndipo anati, nanena naye, Mutiuze muchita izi ndi ulamuliro wotani? Kapena ndani iye amene anakupatsani ulamuliro umene?


Ubatizo wa Yohane unachokera Kumwamba kodi, kapena kwa anthu?


ndipo ndikakufunsani kanthu, simudzayankha.


Mau anu akhale m'chisomo, okoleretsa, kuti mukadziwe inu mayankhidwe anu a kwa yense akatani.