Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 1:57 - Buku Lopatulika

Ndipo inakwanira nthawi ya Elizabeti, ya kubala kwake, ndipo anabala mwana wamwamuna.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo inakwanira nthawi ya Elizabeti, ya kubala kwake, ndipo anabala mwana wamwamuna.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthaŵi yakuti Elizabeti achire idakwana, ndipo adabala mwana wamwamuna.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Itakwana nthawi yoti Elizabeti abereke, anabereka mwana wamwamuna.

Onani mutuwo



Luka 1:57
7 Mawu Ofanana  

Mulungu sindiye munthu, kuti aname; kapena mwana wa munthu, kuti aleke; kodi anena, osachita?


Koma mngelo anati kwa iye, Usaope Zekariya, chifukwa kuti lamveka pemphero lako, ndipo mkazi wako Elizabeti adzakubalira mwana wamwamuna, ndipo udzamutcha dzina lake Yohane.


Masiku a Herode, mfumu ya Yudeya, kunali munthu wansembe, dzina lake Zakariya, wa gulu la ansembe la Abiya; ndi mkazi wake wa ana aakazi a fuko la Aroni, dzina lake Elizabeti.


Ndipo Maria anakhala ndi iye ngati miyezi itatu, nabweranso kunyumba kwake.


Ndipo anansi ake ndi abale ake anamva kuti Ambuye anakulitsa chifundo chake pa iye; nakondwera naye pamodzi.