Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 9:14 - Buku Lopatulika

Ndipo padzakhala pophimba ndi mtambo Ine dziko lapansi, utawo udzaoneka m'mtambomo;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo padzakhala pophimba ndi mtambo Ine dziko lapansi, utawo udzaoneka m'mtambomo;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthaŵi zonse pakakhala mitambo mu mlengalenga, ndipo pakaoneka utawaleza m'mitambomo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nthawi zonse pakakhala mitambo mu mlengalenga ndipo utawaleza uwoneka,

Onani mutuwo



Genesis 9:14
3 Mawu Ofanana  

ndiika utawaleza wanga m'mtambomo, ndipo udzakhala chizindikiro cha pangano lopangana ndi Ine ndi dziko lapansi.


ndipo ndidzakumbukira pangano langa limene lili ndi Ine ndi inu, ndi zamoyo zonse zokhala ndi moyo; ndipo madzi sadzakhalanso konse chigumula chakuononga zamoyo zonse.


Amene aphimba thambo ndi mitambo, amene akonzera mvula nthaka, amene aphukitsa msipu pamapiri.