Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 6:1 - Buku Lopatulika

Ndipo panali pamene anthu anayamba kuchuluka padziko, ndi ana aakazi anawabadwira iwo,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo panali pamene anthu anayamba kuchuluka padziko, ndi ana akazi anawabadwira iwo,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthaŵi imeneyo anthu anali atayamba kuchuluka pa dziko lonse lapansi, ndipo adabereka ana aakazi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu atayamba kuchuluka pa dziko lapansi ndi kubereka ana aakazi,

Onani mutuwo



Genesis 6:1
3 Mawu Ofanana  

Mulungu ndipo anadalitsa iwo, ndipo adati kwa iwo, Mubalane, muchuluke, mudzaze dziko lapansi, muligonjetse: mulamulire pansomba za m'nyanja, ndi pambalame za m'mlengalenga, ndi pazamoyo zonse zokwawa padziko lapansi.


Ndipo Nowa anali wa zaka mazana asanu; ndipo Nowa anabala Semu ndi Hamu ndi Yafeti.


kuti ana aamuna a Mulungu anayang'ana ana aakazi a anthu, kuti iwo anali okongola; ndipo anadzitengera okha akazi onse amene anawasankha.