Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:9 - Buku Lopatulika

Ndipo Enosi anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi anai, nabala Kenani;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Enosi anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi anai, nabala Kenani;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Enosi ali wa zaka 90, adabereka mwana dzina lake Kenani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Enosi anali ndi zaka 90, anabereka Kenani.

Onani mutuwo



Genesis 5:9
4 Mawu Ofanana  

ndipo anakhala ndi moyo Enosi, atabala Kenani, zaka mazana asanu ndi atatu kudza khumi ndi zisanu: ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi.


masiku ake onse a Seti anali zaka mazana asanu ndi anai kudza khumi ndi ziwiri; ndipo anamwalira.


Kenani, Mahalalele, Yaredi,


mwana wa Metusela, mwana wa Enoki, mwana wa Yaredi, mwana wa Mahalalele, mwana wa Kainani,