Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:10 - Buku Lopatulika

ndipo anakhala ndi moyo Enosi, atabala Kenani, zaka mazana asanu ndi atatu kudza khumi ndi zisanu: ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo anakhala ndi moyo Enosi, atabala Kenani, zaka mazana asanu ndi atatu kudza khumi ndi zisanu: ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo adakhalanso ndi moyo zaka zina 815. Adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atabadwa Kenani, Enosi anakhala ndi moyo zaka zina 815 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo



Genesis 5:10
3 Mawu Ofanana  

Masiku ake onse a Enosi anali mazana asanu ndi anai kudza zisanu; ndipo anamwalira.


Masiku ake Adamu atabala Seti, anali zaka mazana asanu ndi atatu; ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi.


Ndipo Enosi anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi anai, nabala Kenani;