Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 48:8 - Buku Lopatulika

Ndipo Israele anayang'ana ana aamuna a Yosefe, nati, Ndani awa?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Israele anayang'ana ana amuna a Yosefe, nati, Ndani awa?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yakobe ataona ana a Yosefe, adafunsa kuti, “Nanga anyamata aŵa nga yani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Israeli ataona ana a Yosefe anafunsa kuti, “Anyamatawa ndi a yani?”

Onani mutuwo



Genesis 48:8
3 Mawu Ofanana  

Koma maso a Israele anali akhungu mu ukalamba wake, ndipo sanathei kuona. Ndipo anadza nao pafupi; ndipo anapsompsona iwo, nawafungatira.


Ndipo Yosefe anati kwa atate wake, Amenewa ndi ana anga, amene Mulungu wandipatsa ine pano. Ndipo iye anati, Udze naotu kwa ine, ndipo ndidzawadalitsa.


Funani Yehova, ndipo mudzakhala ndi moyo; angabuke ngati moto m'nyumba ya Yosefe, ndipo unganyeke wopanda wakuzima mu Betele;