Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 41:44 - Buku Lopatulika

Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Ine ndine Farao, ndipo popanda iwe palibe munthu aliyense adzatukula dzanja lake kapena mwendo wake m'dziko lonse la Ejipito.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Ine ndine Farao, ndipo popanda iwe palibe munthu aliyense adzatukula dzanja lake kapena mwendo wake m'dziko lonse la Ejipito.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Farao adauza Yosefe kuti, “Pali ine ndemwe Farao, iwe ukapanda kulola, palibe ndi mmodzi yemwe amene adzathe kuchita kanthu kalikonse ngakhale kuyenda kumene m'dziko la Ejipito lonseli.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka Farao anati kwa Yosefe, “Ine ndine Farao; tsono iwe ukapanda kulamula, palibe amene akhoza kuchita chilichonse ngakhale kuyenda kumene mʼdziko lonse la Igupto.”

Onani mutuwo



Genesis 41:44
4 Mawu Ofanana  

ndipo anamkweza iye m'galeta wake wachiwiri amene anali naye: ndipo anafuula patsogolo pa iye, Gwadani; ndipo anamkhazika iye wolamulira dziko lonse la Ejipito.


Pakuti Mordekai Myuda anatsatana naye mfumu Ahasuwero, nakhala wamkulu mwa Ayuda, navomerezeka mwa unyinji wa abale ake wakufunira a mtundu wake zokoma, ndi wakunena za mtendere kwa mbeu yake yonse.


Amange nduna zake iye mwini, alangize akulu ake adziwe nzeru.


Koma palibe galu adzafunyitsira lilime lake ana onse a Israele ngakhale anthu kapena zoweta; kuti mudziwe kuti Yehova asiyanitsa pakati pa Aejipito ndi Aisraele.