Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 27:10 - Buku Lopatulika

ndipo udzapita nacho kwa atate wako, kuti adye, ndi kukudalitsa iwe asanafe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo udzapita nacho kwa atate wako, kuti adye, ndi kukudalitsa iwe asanafe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ukapereke chakudyacho kwa bambo wako kuti akadye, ndipo akudalitse asanafe.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka upite nacho chakudyacho kwa abambo ako kuti adye ndi kukudalitsa asanafe.”

Onani mutuwo



Genesis 27:10
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anati, Yehova, Mulungu wa mbuyanga Abrahamu mundiyendetse ine bwino lero lino, mumchitire ufulu mbuyanga Abrahamu.


Yakobo ndipo anati kwa Rebeka amake, Taonani, Esau mkulu wanga ndiye munthu waubweya, ine ndine munthu wosalala.


Pitatu kubusa, ukanditengere ine kumeneko tiana tiwiri tabwino tambuzi; ndikonzere nato chakudya chokolera cha atate wako chonga chomwe achikonda: