Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 26:6 - Buku Lopatulika

Ndipo Isaki anakhala mu Gerari;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Isaki anakhala m'Gerari;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero Isaki adakhala ku Gerari.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Isake anakhala ku Gerari.

Onani mutuwo



Genesis 26:6
3 Mawu Ofanana  

Abrahamu ndipo anachoka kumeneko kunka ku dziko la kumwera, ndipo anakhala pakati pa Kadesi ndi Suri, ndipo anakhala ngati mlendo mu Gerari.


chifukwa kuti Abrahamu anamvera mau anga, nasunga chilangizo changa, ndi maweruziro anga, ndi malemba anga ndi malamulo anga.


ndipo anthu a kumeneko anamfunsa iye za mkazi wake; ndipo iye anati, Ndiye mlongo wanga: chifukwa kuti anaopa kunena, Mkazi wanga; anati, anthu a kumeneko angandiphe ine chifukwa cha Rebeka; popeza anali wokongola pakumuona.