Genesis 26:5 - Buku Lopatulika5 chifukwa kuti Abrahamu anamvera mau anga, nasunga chilangizo changa, ndi maweruziro anga, ndi malemba anga ndi malamulo anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 chifukwa kuti Abrahamu anamvera mau anga, nasunga chilangizo changa, ndi maweruziro anga, ndi malemba anga ndi malamulo anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndidzakudalitsa iwe chifukwa Abrahamu adandimvera, ndipo adatsata malamulo ndi malangizo anga onse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 chifukwa Abrahamu anandimvera, nasunga malamulo anga onse.” Onani mutuwo |