Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 22:10 - Buku Lopatulika

Ndipo Abrahamu anatambasula dzanja lake, natenga mpeni kuti amuphe mwana wake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Abrahamu anatambasula dzanja lake, natenga mpeni kuti amuphe mwana wake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono adasolola mpeni kuti amuphe mwana wakeyo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka Abrahamu anatambasula dzanja lake natenga mpeni kuti aphe mwana wake.

Onani mutuwo



Genesis 22:10
6 Mawu Ofanana  

Koma mthenga wa Yehova anamuitana iye ndi mau odzera kumwamba, nati, Abrahamu, Abrahamu; ndi iye anati, Ndine pano.


m'mbeu zako mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsidwa: chifukwa wamvera mau anga.


Ndipo anafika kumalo komwe Mulungu anamuuza iye; ndipo Abrahamu anamanga guwa la nsembe nakonza nkhuni, namanga Isaki mwana wake, namuika iye paguwa la nsembe pamwamba pa nkhuni.