Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 11:17 - Buku Lopatulika

ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza makumi awiri, atabala Pelegi, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza makumi awiri, atabala Pelegi, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake adakhala ndi moyo zaka zina 430, ndipo adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atabereka Pelegi, Eberi anakhala ndi moyo zaka zina 430 ndipo anali ndi ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo



Genesis 11:17
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza zinai, nabala Pelegi;


Ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Reu;