Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 11:12 - Buku Lopatulika

Ndipo Aripakisadi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza zisanu nabala Sela;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Aripakisadi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza zisanu nabala Sela;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene Aripakisadi anali wa zaka 35, adabereka mwana dzina lake Sela.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Aripakisadi anali ndi zaka 35, anabereka Sela.

Onani mutuwo



Genesis 11:12
5 Mawu Ofanana  

Aripakisadi ndipo anabala Sela; ndipo Sela anabala Eberi.


ndipo Semu anakhala ndi moyo zaka mazana asanu, atabala Aripakisadi, nabala ana aamuna ndi aakazi.


ndipo Aripakisadi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza zitatu, atabala Sela, nabala ana aamuna ndi aakazi.


Ndi Aripakisadi anabala Sela; ndi Sela anabala Eberi.


mwana wa Kainani, mwana wa Arifaksadi, mwana wa Semu, mwana wa Nowa, mwana wa Lameki,