Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 10:30 - Buku Lopatulika

Kwao kunayamba pa Mesa pakunka ku Sefari phiri la kum'mawa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kwao kunayamba pa Mesa pakunka ku Sefari phiri la kum'mawa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Dziko limene ankakhalamo lidayambira ku Mesa kumaloŵa ku Sefari ku mapiri chakuvuma.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chigawo chimene ankakhala chinayambira ku Mesa mpaka ku Seferi, ku dera la mapiri chakummawa.

Onani mutuwo



Genesis 10:30
3 Mawu Ofanana  

ndi Ofiri ndi Havila, ndi Yobabu; onse amenewa ndi ana a Yokotani.


Amenewa ndi ana a Semu, monga mwa mabanja ao, mwa zinenedwe zao, m'maiko ao, m'mitundu yao.


Ndipo ananena fanizo lake, nati, Ku Aramu ananditenga Balaki, mfumu ya Mowabu ananditenga ku mapiri a kum'mawa, Idza, udzanditembererere Yakobo. Idza, nudzanyoze Israele.