Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 10:3 - Buku Lopatulika

Ndi ana aamuna a Gomeri: Asikenazi, ndi Rifati, ndi Togarima.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi ana amuna a Gomeri: Asikenazi, ndi Rifati, ndi Togarima.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana a Gomeri anali Asikenazi, Rifati ndi Togarima.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima.

Onani mutuwo



Genesis 10:3
4 Mawu Ofanana  

Ndi ana a Gomeri: Asikenazi, Difati, ndi Togarima.


Kwezani mbendera m'dziko, ombani lipenga mwa amitundu, konzerani amitundu amenyane naye, mummemezere maufumu a Ararati, Mini, ndi Asikenazi; muike nduna; amenyane naye; mukweretse akavalo ngati dzombe.


Iwo a nyumba ya Togarima anagula malonda ako ndi akavalo, ndi akavalo a nkhondo, ndi nyuru.


Gomeri ndi magulu ake onse, nyumba ya Togarima, ku malekezero a kumpoto, ndi magulu ake onse, mitundu yambiri pamodzi ndi iwe.