Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 10:23 - Buku Lopatulika

Ndi ana a Aramu: Uzi ndi Huli ndi Getere, ndi Masi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi ana a Aramu: Uzi ndi Huli ndi Getere, ndi Masi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana a Aramu anali Uzi, Hulu, Getere ndi Masi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.

Onani mutuwo



Genesis 10:23
3 Mawu Ofanana  

Ana a Semu: Elamu, ndi Asiriya, ndi Aripakisadi, ndi Ludi, ndi Aramu, ndi Uzi, ndi Huli, ndi Getere, ndi Meseki.


Panali munthu m'dziko la Uzi, dzina lake ndiye Yobu; ndipo munthuyu anali wangwiro ndi woongoka, wakuopa Mulungu ndi kupewa zoipa.


ndi anthu onse osakanizidwa, ndi mafumu onse a dziko la Uzi, ndi mafumu onse a dziko la Afilisti, ndi Asikeloni, ndi Gaza, ndi Ekeroni, ndi otsala a Asidodi,