Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 10:12 - Buku Lopatulika

ndi Reseni pakati pa Ninive ndi Kala: umenewo ndi mzinda waukulu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Reseni pakati pa Ninive ndi Kala: umenewo ndi mudzi waukulu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndi mzinda wa Reseni umene uli pakati pa Ninive ndi mzinda waukulu uja wa Kala.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndi Reseni, mzinda waukulu umene uli pakati pa Ninive ndi Kala.

Onani mutuwo



Genesis 10:12
3 Mawu Ofanana  

M'dziko momwemo iye anatuluka kunka ku Asiriya, namanga Ninive, ndi mzinda wa Rehoboti, ndi Kala,


Ejipito ndipo anabala Ludimu, ndi Anamimu, ndi Lehabu, ndi Nafituhimu,


Meseki, Tubala, ndi aunyinji ake onse ali komweko, manda ake amzinga; onsewo osadulidwa, ophedwa ndi lupanga; pakuti anaopsetsa m'dziko la amoyo.