Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 9:30 - Buku Lopatulika

Koma inu ndi anyamata anu ndidziwa kuti simudzayamba kuopa nkhope ya Yehova Mulungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma inu ndi anyamata anu ndidziwa kuti simudzayamba kuopa nkhope ya Yehova Mulungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komabe ndikudziŵa kuti inu ndi nduna zanu simukuwopa Chauta.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma ine ndikudziwa kuti inu ndi nduna zanu simukuopabe Yehova Mulungu.”

Onani mutuwo



Eksodo 9:30
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anati, Onani, ndilikutuluka ine kwanu, ndidzapemba Yehova kuti mizaza ichoke mawa kwa Farao, ndi kwa anyamata ake, ndi kwa anthu ake; komatu, Farao asanyengenso ndi kukana kulola anthuwa amuke kukamphera nsembe Yehova.


Mphulupulu iomboledwa ndi chifundo ndi ntheradi; apatuka pa zoipa poopa Yehova.


Ungayanje woipa, koma sadzaphunzira chilungamo; m'dziko la machitidwe oongoka, iye adzangochimwa, sadzaona chifumu cha Yehova.


Yehova bwanji mwatisocheretsa kusiya njira zanu, ndi kuumitsa mitima yathu tisakuopeni? Bwerani, chifukwa cha atumiki anu, mafuko a cholowa chanu.