Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 36:16 - Buku Lopatulika

Ndipo anamanga pamodzi nsalu zisanu pazokha, ndi nsalu zisanu ndi imodzi pazokha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anamanga pamodzi nsalu zisanu pa zokha, ndi nsalu zisanu ndi imodzi pa zokha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono adasokerera nsalu zisanu nkukhala chinsalu chimodzi, ndipo nsalu zinazo zisanu ndi imodzi, adazisokereranso kuti zikhale chinsalu chimodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo analumikiza nsalu zisanu kukhala nsalu imodzi ndipo nsalu zinazo zisanu ndi imodzi, analumikizanso kukhala nsalu imodzinso.

Onani mutuwo



Eksodo 36:16
2 Mawu Ofanana  

Utali wake wa nsalu imodzi ndiwo mikono makumi atatu, ndi kupingasa kwake kwa nsalu imodzi ndiko mikono inai; nsalu khumi ndi imodzi zinafanana muyeso wao.


Ndipo anapanga magango makumi asanu m'mphepete mwa nsalu imodzi, ya kuthungo, ya chilumikizano, naika magango makumi asanu m'mphepete mwa nsalu ya kuthungo, ya chilumikizano china.