Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 29:6 - Buku Lopatulika

ndipo uike nduwira pamutu pake, ndi kuika korona wopatulika panduwirapo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo uike nduwira pamutu pake, ndi kuika korona wopatulika panduwirapo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Umuveke nduŵira kumutu kwake, ndi duŵa lopatulika lija panduŵirapo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Umuveke nduwira kumutu, ndiponso uyike chizindikiro chopatulika chija pa nduwirayo.

Onani mutuwo



Eksodo 29:6
5 Mawu Ofanana  

Ndipo zovala azisoka ndi izi: chapachifuwa ndi efodi, ndi mwinjiro, ndi malaya opikapika, ndi nduwira, ndi mpango; tero apangire Aroni mbale wako ndi ana ake zovala zopatulika, kuti andichitire Ine ntchito ya nsembe.


Asatuluke m'malo opatulika, kapena kuipsa malo opatulika a Mulungu wake; popeza korona wa mafuta odzoza wa Mulungu wake ali pa iye; Ine ndine Yehova.


Naika nduwirayo pamutu pake; ndi panduwira, pamphumi pake anaika golide waphanthiphanthi, ndiwo korona wopatulika; monga Yehova adauza Mose.


Ndipo ndinati, Amuike nduwira yoyera pamutu pake. Naika nduwira yoyera pamutu pake, namveka ndi zovala; ndi mthenga wa Yehova anaimirirapo.