Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 28:23 - Buku Lopatulika

Nupangire pa chapachifuwa mphete ziwiri zagolide, ndi kuzika mphete ziwirizo pansonga zake ziwiri za chapachifuwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nupangire pa chapachifuwa mphete ziwiri zagolide, ndi kuzika mphete ziwirizo pa nsonga zake ziwiri za chapachifuwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Upangenso mphete ziŵiri, ndipo uzilumikize pa ngodya zam'mwamba za chovala chapachifuwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Upangenso mphete ziwiri zagolide ndipo uzimangirire pa ngodya ziwiri za pa chovala chapachifuwa.

Onani mutuwo



Eksodo 28:23
3 Mawu Ofanana  

Upangenso maunyolo pa chapachifuwa ngati zingwe, ntchito yopota, ya golide woona.


Numange maunyolo awiri opota agolide ku mphete ziwirizo pansonga pake pa chapachifuwa.