Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 27:13 - Buku Lopatulika

Ndipo m'kupingasa kwake kwa bwalo pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mukhale mikono makumi asanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo m'kupingasa kwake kwa bwalo pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mukhale mikono makumi asanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chakuvuma, komwe kuli chipata chake, bwalolo likhalenso mamita 23 muufupi mwake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mbali yakummawa, kotulukira dzuwa, kutalika kwa bwalo kukhale mamita 23.

Onani mutuwo



Eksodo 27:13
2 Mawu Ofanana  

Ndipo m'kupingasa kwa bwaloli pa mbali ya kumadzulo mukhale nsalu zotchingira za mikono makumi asanu; nsichi zake zikhale khumi, ndi makamwa ao khumi.


Ndi nsalu zotchingira za pa mbali imodzi ya kuchipata zikhale za mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zikhale zitatu, ndi makamwa ao atatu.