Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 26:16 - Buku Lopatulika

Utali wake wa thabwa limodzi ndiwo mikono khumi, ndi kupingasa kwake kwa thabwali mkono ndi hafu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Utali wake wa thabwa limodzi ndiwo mikono khumi, ndi kupingasa kwake kwa thabwali mkono ndi hafu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Muutali mwake fulemu lililonse likhale mamita anai ndi theka, ndipo muufupi mwake masentimita 69.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Feremu iliyonse ikhale yotalika mamita anayi ndipo mulifupi mwake mukhale masentimita 69.

Onani mutuwo



Eksodo 26:16
2 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipangira chihema matabwa oimirika, a mtengo wakasiya.


Pa thabwa limodzi pakhale mitsukwa iwiri, yomangika pamodzi; uzitero pa matabwa onse a chihema.