Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 23:3 - Buku Lopatulika

kapena usakometsera munthu wosauka pa mlandu wake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kapena usakometsera munthu wosauka pa mlandu wake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu wosauka ukamuweruza, usaweruze mokondera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo poweruza mlandu wa munthu wosauka usamukondere.

Onani mutuwo



Eksodo 23:3
10 Mawu Ofanana  

Usakhotetsa mlandu wa mnzako waumphawi.


Kukometsa mlandu wa wamphulupulu mwatsankho sikuli kwabwino, ngakhale kuchitira chetera wolungama.


Usalande za waumphawi chifukwa ali waumphawi, ngakhale kutsendereza wosauka kubwalo.


Tsoka kwa iwo amene alamulira malamulo osalungama, ndi kwa alembi olemba mphulupulu;


Musamachita chisalungamo pakuweruza mlandu; usamavomereza munthu wosauka, kapena kulemekeza munthu womveka; uweruze mlandu wa munthu mnzako molungama.


Pakuti ndidziwa kuti zolakwa zanu nzochuluka, ndi machimo anu ndi olimba, inu akusautsa olungama, akulandira chokometsera mlandu, akukankha osowa kuchipata.


Musamasamalira munthu poweruza mlandu; ang'ono ndi akulu muwamvere chimodzimodzi; musamaopa nkhope ya munthu; popeza chiweruzo ncha Mulungu; ndipo mlandu ukakukanikani mubwere nao kwa ine, ndidzaumva.


Musamapotoza chiweruzo, musamasamalira munthu, kapena kulandira chokometsera mlandu; popeza chokometsera mlandu chidetsa maso a anzeru, ndi kuipisa mau a olungama.


Koma nzeru yochokera kumwamba iyamba kukhala yoyera, nikhalanso yamtendere, yaulere, yomvera bwino, yodzala chifundo ndi zipatso zabwino, yopanda tsankho, yosadzikometsera pamaso.