Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 21:27 - Buku Lopatulika

Ndipo akagulula dzino la mnyamata wake, kapena dzino la mdzakazi wake, azimlola amuke waufulu chifukwa cha dzino lake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo akagulula dzino la mnyamata wake, kapena dzino la mdzakazi wake, azimlola amuke waufulu chifukwa cha dzino lake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akamchotsa dzino, ammasule kapoloyo, kuti akhale mfulu chifukwa cha dzinolo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo ngati agulula dzino la wantchito wamwamuna kapena mdzakazi, wantchitoyo amasulidwe ngati malipiro a dzino lake.

Onani mutuwo



Eksodo 21:27
2 Mawu Ofanana  

Munthu akampanda mnyamata wake, kapena mdzakazi wake, padiso, nalithudzula, azimlola amuke waufulu chifukwa cha diso lake.


Ng'ombe ikatunga mwamuna kapena mkazi, nafa, aiponyetu miyala ng'ombeyo, osadya nyama yake; koma mwini ng'ombeyo azimasuka.