Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 21:15 - Buku Lopatulika

Munthu wakukantha atate wake, kapena amai wake, aphedwe ndithu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Munthu wakukantha atate wake, kapena amai wake, aphedwe ndithu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Munthu aliyense amene amenya bambo wake kapena mai wake, aphedwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Munthu aliyense amene amenya abambo ake kapena mayi ake ayenera kuphedwa.

Onani mutuwo



Eksodo 21:15
7 Mawu Ofanana  

Koma munthu akachita dala pa mnzake, kumupha monyenga; uzimchotsa ku guwa langa la nsembe, kuti afe.


Iye wakuba munthu, angakhale wamgulitsa, kapena akampeza m'dzanja lake, aphedwe ndithu.


Pali mbadwo wotemberera atate ao, osadalitsa amai ao.


Diso lochitira atate wake chiphwete, ndi kunyoza kumvera amake, makwangwala a kumtsinje adzalikolowola, ana a mphungu adzalidya.


Wotembereredwa iye wakukantha mnansi wake m'tseri. Ndi anthu onse anene, Amen.


podziwa ichi, kuti lamulo siliikika kwa munthu wolungama, koma kwa osaweruzika ndi osamvera lamulo, osapembedza, ndi ochimwa, osalemekeza ndi amnyozo, akupha atate ndi akupha amai, akupha anzao,