Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 21:11 - Buku Lopatulika

Ndipo akapanda kumchitira izi zitatu, azituluka chabe, osaperekapo ndalama.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo akapanda kumchitira izi zitatu, azituluka chabe, osaperekapo ndalama.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akapanda kumchitira zimenezi, ammasule kuti akhale mfulu, koma osalandirapo ndalama.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma ngati sangathe kumuchitira zonsezi, ndiye amuleke apite popanda kulipira kanthu.

Onani mutuwo



Eksodo 21:11
2 Mawu Ofanana  

Akamtengera mkazi wina, asachepetse chakudya chake, zovala zake, ndi za ukwati zakezake.


Iye amene akantha munthu kotero kuti wafa, aphedwe ndithu.