Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 1:4 - Buku Lopatulika

Dani ndi Nafutali, Gadi ndi Asere.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Dani ndi Nafutali, Gadi ndi Asere.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Dani, Nafutali, Gadi ndi Asere.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Dani, Nafutali; Gadi ndi Aseri.

Onani mutuwo



Eksodo 1:4
4 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Israele anakhala m'dzikomo, Rubeni anamuka nagona ndi Biliha, mkazi wamng'ono wa atate wake: ndipo Israele anamva. Ana aamuna a Yakobo anali khumi ndi awiri:


Amenewa ndi ana a Zilipa, amene Labani anampatsa Leya mwana wake wamkazi, amenewo anambalira Yakobo, anthu khumi ndi asanu ndi mmodzi.


Isakara, Zebuloni, ndi Benjamini;


Ndipo amoyo onse amene anatuluka m'chuuno mwake mwa Yakobo ndiwo makumi asanu ndi awiri; koma Yosefe anali mu Ejipito.