Genesis 46:18 - Buku Lopatulika18 Amenewa ndi ana a Zilipa, amene Labani anampatsa Leya mwana wake wamkazi, amenewo anambalira Yakobo, anthu khumi ndi asanu ndi mmodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Amenewa ndi ana a Zilipa, amene Labani anampatsa Leya mwana wake wamkazi, amenewo anambalira Yakobo, anthu khumi ndi asanu ndi mmodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 (Onseŵa anali adzukulu a Yakobe obadwa mwa Zilipa amene Labani adaapereka kwa mwana wake Leya.) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Amenewa ndi zidzukulu za Yakobo mwa Zilipa amene Labani anapereka kwa mwana wake, Leya. Onse pamodzi analipo 16. Onani mutuwo |