Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 2:36 - Buku Lopatulika

Ili ndi loto; kumasulira kwake tsono tikufotokozerani mfumu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ili ndi loto; kumasulira kwake tsono tikufotokozerani mfumu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Maloto aja ndi amenewa; tidzafotokoza tanthauzo lake kwa mfumu.

Onani mutuwo



Danieli 2:36
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yosefe anati kwa iye, Kumasulira kwake ndi uwu: nthambi zitatu ndizo masiku atatu;


Ndipo Yosefe anayankha nati, Kumasulira kwake ndi uku: malichero atatu ndiwo masiku atatu;


Inu mfumu munapenya ndi kuona fano lalikulu. Fanoli linali lalikulu, ndi kunyezimira kwake kunaposa; linali kuima popenyana ndi inu, ndi maonekedwe ake anali oopsa.