Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 11:19 - Buku Lopatulika

Pamenepo adzatembenuzira nkhope yake kumalinga a dziko lakelake; koma adzakhumudwa, nadzagwa osapezedwanso.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo adzatembenuzira nkhope yake kumalinga a dziko lakelake; koma adzakhumudwa, nadzagwa osapezedwanso.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zikadzatha izi, mfumu idzabwerera ku malo otetezedwa a dziko la kwawo koma idzapunthwa ndi kugwa osapezekanso.

Onani mutuwo



Danieli 11:19
9 Mawu Ofanana  

Adzauluka ngati loto, osapezekanso; nadzaingidwa ngati masomphenya a usiku.


Aphwanya eni mphamvu osatulutsa kubwalo mlandu wao, naika ena m'malo mwao.


Pondifika ine ochita zoipa kudzadya mnofu wanga, inde akundisautsa ndi adani anga, anakhumudwa iwo nagwa.


Ndapenya woipa, alikuopsa, natasa monga mtengo wauwisi wanzika.


Koma anapita ndipo taona, kwati zii; ndipo ndinampwaira osampeza.


Dziko lapansi lidzachita dzandidzandi, ngati munthu woledzera, ndi kunjenjemera, ngati chilindo; ndi kulakwa kwake kudzalilemera, ndipo lidzagwa losaukanso.


Waliwiro asathawe, wamphamvu asapulumuke; kumpoto pambali pamtsinje wa Yufurate waphunthwa nagwa.


ndidzakuika woopsa; ndipo sudzaonekanso, chinkana akufunafuna sudzapezekanso konse, ati Ambuye Yehova.


Koma apo pophukira mizu yake adzauka wina m'malo mwake, ndiye adzafika kulimbana nalo khamu la nkhondo, nadzalowa m'linga la mfumu ya kumpoto, nadzachita molimbana nao, nadzawagonjetsa;