Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Afilipi 2:18 - Buku Lopatulika

momwemonso kondwerani inu, nimukondwere pamodzi ndi ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

momwemonso kondwerani inu, nimukondwere pamodzi ndi ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chimodzimodzi inunso muzikondwa, ndi kusangalala nane pamodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chomwechonso, inu khalani okondwa ndi osangalala nane pamodzi.

Onani mutuwo



Afilipi 2:18
6 Mawu Ofanana  

Mwa ichi ndipempha kuti musade mtima m'zisautso zanga chifukwa cha inu, ndiwo ulemerero wanu.


Komatu ngatinso ndithiridwa pa nsembe ndi kutumikira kwa chikhulupiriro chanu, ndikondwera, ndipo ndikondwera pamodzi ndi inu nonse;


Koma ndiyembekeza mwa Ambuye Yesu kuti ndidzatumiza Timoteo kwa inu msanga, kuti inenso nditonthozeke bwino pozindikira za kwa inu.


Chotsalira, abale anga, kondwerani mwa Ambuye. Kulembera zomwezo kwa inu, sikundivuta ine, koma kwa inu kuli kukhazikitsa.


Kondwerani mwa Ambuye nthawi zonse: ndibwerezanso kutero, kondwerani.