Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Afilipi 1:24 - Buku Lopatulika

koma kukhalabe m'thupi ndiko kufunika koposa, chifukwa cha inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma kukhalabe m'thupi ndiko kufunika koposa, chifukwa cha inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma kwinakunso nkofunika kwambiri kuti ndikhale moyo chifukwa cha inuyo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Komanso nʼkofunika kwambiri kuti ndikhalebe mʼthupi chifukwa cha inu.

Onani mutuwo



Afilipi 1:24
5 Mawu Ofanana  

Koma ndinena Ine choonadi ndi inu; kuyenera kwa inu kuti ndichoke Ine; pakuti ngati sindichoka, Nkhosweyo sadzadza kwa inu; koma ngati ndipita ndidzamtuma Iye kwa inu.


Koma ngati kukhala ndi moyo m'thupi ndiko chipatso cha ntchito yanga, sindizindikiranso chimene ndidzasankha.


Koma ndipanidwa nazo ziwirizi, pokhala nacho cholakalaka cha kuchoka kukhala ndi Khristu, ndiko kwabwino koposaposatu;