Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 3:2 - Buku Lopatulika

Ndipo ana a Davide anabadwira ku Hebroni. Mwana woyamba ndiye Aminoni, wa Ahinowamu wa ku Yezireele;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ana a Davide anabadwira ku Hebroni. Mwana woyamba ndiye Aminoni, wa Ahinowamu wa ku Yezireele;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Davide adabereka ana aamuna ku Hebroni. Mwana wake woyamba anali Aminoni, wobadwa kwa Ahinowamu wa ku Yezireele.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ana aamuna a Davide amene anabadwira ku Hebroni anali awa: Woyamba anali Amnoni, amayi ake anali Ahinoamu wa ku Yezireeli.

Onani mutuwo



2 Samueli 3:2
6 Mawu Ofanana  

Wolemerayo anali nazo zoweta zazing'ono ndi zazikulu zambiri ndithu;


Ndipo kunali pakutha zaka zinai Abisalomu ananena kwa mfumu, Mundilole ndimuke ku Hebroni ndikachite chowinda changa ndinachiwindira Yehova.