Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 23:30 - Buku Lopatulika

Benaya Mpiratoni, Hidai wa ku timitsinje ta Gaasi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Benaya Mpiratoni, Hidai wa ku timitsinje ta Gaasi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Panalinso Benaya wa ku Piratoni, Hidai wa ku mitsinje ya ku Gaasi,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Benaya Mpiratoni, Hidayi wa ku zigwa za Gaasi.

Onani mutuwo



2 Samueli 23:30
7 Mawu Ofanana  

Wakhumi ndi chimodzi wa mwezi wakhumi ndi chimodzi ndiye Benaya Mpiratoni wa ana a Efuremu; ndi m'chigawo mwake zikwi makumi awiri mphambu zinai.


amenewa anatembenuka nakwera kumapiri nalowa ku chigwa cha Esikolo, nachizonda.


Ndipo anamuika m'malire a cholowa chake mu Timnati-Sera, ndiwo ku mapiri a Efuremu kumpoto kwa phiri la Gaasi.


Ndi pambuyo pake Abidoni mwana wa Hilele wa ku Piratoni anaweruza Israele.


Nafa Abidoni mwana wa Hilele wa ku Piratoni, naikidwa mu Piratoni m'dziko la Efuremu ku mapiri a Amaleke.


Ndipo anamuika m'malire a cholowa chake mu Timnati-Heresi, ku mapiri a Efuremu, kumpoto kwa phiri la Gaasi.