Oweruza 2:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo anamuika m'malire a cholowa chake mu Timnati-Heresi, ku mapiri a Efuremu, kumpoto kwa phiri la Gaasi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo anamuika m'malire a cholowa chake m'Timnati-Heresi, ku mapiri a Efuremu, kumpoto kwa phiri la Gaasi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndipo adamuika m'dziko lake limene adalandira ngati choloŵa chake ku Timnati-Heresi m'dziko lamapiri la Efuremu, kumpoto kwa phiri la Gaasi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo anamuyika mʼmanda a mʼdziko lake, ku Timnati-Heresi mʼdziko la mapiri la Efereimu, kumpoto kwa phiri la Gaasi. Onani mutuwo |