Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 18:30 - Buku Lopatulika

Ndipo mfumu inati, Patuka nuime apa. Napatuka, naimapo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mfumu inati, Patuka nuime apa. Napatuka, naimapo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pompo mfumu idati, “Patuka, kaime apo.” Iye adapatuka nakaima potero.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mfumu inati, “Ima apo ndipo udikire.” Kotero iye anapita pa mbali nayima pamenepo.

Onani mutuwo



2 Samueli 18:30
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu inati, Kodi mnyamatayo Abisalomu ali bwino? Ahimaazi nayankha, Pamene Yowabu anatumiza mnyamata wa mfumu, ndiye ine mnyamata wanu, ndinaona piringupiringu, koma sindinadziwe ngati kutani.


Ndipo onani, Mkusiyo anafika, nati, Mau akuuza mbuye wanga mfumu; pakuti Yehova anabwezera chilango lero onse akuukira inu.