Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 12:29 - Buku Lopatulika

Ndipo Davide anasonkhanitsa anthu onse, napita ku Raba, naponyana nao, naulanda.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Davide anasonkhanitsa anthu onse, napita ku Raba, naponyana nao, naulanda.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho Davide adasonkhanitsa ankhondo ake onse, ndipo adapita ku Raba, nakauthira nkhondo mzindawo, nkuulanda.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kotero Davide anasonkhanitsa ankhondo onse ndipo anapita ku Raba kukawuthira nkhondo ndi kuwulanda.

Onani mutuwo



2 Samueli 12:29
3 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake tsono musonkhanitse anthu otsalawo, nimumangire mzindawo zithando, muulande; kuti ine ndingalande mzindawo, ndipo ungatchedwe ndi dzina langa.


Nachotsa korona pamutu wa mfumu yao; kulemera kwake kunali talente wa golide; ndipo m'menemo munali miyala ya mtengo wapatali; ndipo anamuika pamutu wa Davide. Iye natulutsa zofunkha za mzindawo zambirimbiri.


Ndipo kunali pakufika Davide ku Mahanaimu, Sobi mwana wa Nahasi wa ku Raba wa ana a Amoni, ndi Makiri mwana wa Amiyele wa ku Lodebara, ndi Barizilai Mgiliyadi wa ku Rogelimu,