Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 11:5 - Buku Lopatulika

Ndipo mkaziyo anaima, natumiza munthu nauza Davide, kuti Ndili ndi pakati.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mkaziyo anaima, natumiza munthu nauza Davide, kuti Ndili ndi pakati.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kenaka ataona kuti waima, adatumiza mau kwa Davide kukamuuza kuti, “Inetu ndi mommuja, sindili bwino!”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mkaziyo anakhala woyembekezera ndipo anatumiza mawu kwa Davide kunena kuti, “Ine ndine woyembekezera.”

Onani mutuwo



2 Samueli 11:5
4 Mawu Ofanana  

Davide natumiza kwa Yowabu, nati, Unditumizire Uriya Muhiti. Ndipo Yowabu anatumiza Uriya kwa Davide.


Pakuti nsanje ndiyo ukali wa mwamuna, ndipo sadzachitira chifundo tsiku lobwezera chilango.


Munthu akachita chigololo ndi mkazi wa mwini, popeza wachita chigololo ndi mkazi wa mnansi wake, awaphe ndithu, mwamuna ndi mkazi onse awiri.


Akampeza munthu alikugona ndi mkazi wokwatibwa ndi mwamuna; afe onse awiri, mwamuna wakugona ndi mkazi, ndi mkazi yemwe; chotero muzichotsa choipacho mwa Israele.