Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 11:19 - Buku Lopatulika

nauza mthengawo kuti, Utatsiriza kuuza mfumu zonse za nkhondozo;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nauza mthengawo kuti, Utatsiriza kuuza mfumu zonse za nkhondozo;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adauza wamthengayo kuti, “Utatha kumuuza mfumu mbiri yonse ya nkhondo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anamulangiza wa mthengayo kuti, “Pamene ukatsiriza kufotokozera mfumu za ku nkhondozi,

Onani mutuwo



2 Samueli 11:19
2 Mawu Ofanana  

Pamenepo Yowabu anatumiza munthu nauza Davide zonse za nkhondoyi;


kudzali kuti ukapsa mtima wa mfumu nikati kwa iwe, Chifukwa ninji munayandikira pafupi potere pamzinda kukamenyana nao? Simunadziwe kodi kuti apalingawo adzaponya?